Ezara 7:13 BL92

13 Ndilamulira kuti onse a ana a Israyeli, ndi ansembe ao, ndi Alevi, m'ufumu wanga, ofuna eni ace kumuka ku Yerusalemu, apite nawe.

Werengani mutu wathunthu Ezara 7

Onani Ezara 7:13 nkhani