Hoseya 1:4 BL92

4 Ndipo Yehova anati kwa iye, Umuche dzina lace Yezreeli; pakuti katsala kanthawi, ndipo ndidzabwezera cilango mwazi wa Yezreeli pa nyumba ya Yehu, ndi kuleketsa ufumu wa nyumba ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 1

Onani Hoseya 1:4 nkhani