Hoseya 3:1 BL92

1 Ndipo Yehova anati kwa ine, Mukanso, konda mkazi wokondedwa ndi bwenzi lace, koma wakucita cigololo monga Yehova akonda ana a Israyeli, angakhale atembenukira ku milungu yina, nakonda ncinci za mphesa zouma.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 3

Onani Hoseya 3:1 nkhani