Hoseya 7:10 BL92

10 Ndipo kudzikuza kwa Israyeli kumcitira umboni pamaso pace; koma sanabwerera kumka kwa Yehova Mulungu wao, kapena kumfunafuna mwa ici conse.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 7

Onani Hoseya 7:10 nkhani