Hoseya 9:6 BL92

6 Pakuti taonani, anacokera cionongeko, koma Aigupto adzawasonkhanitsa, Mofi adzawaika m'manda; khwisa adzalanda zofunika zao zasiliva; minga idzakhala m'mahema mwao.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 9

Onani Hoseya 9:6 nkhani