Ahebri 11:37 BL92

37 19 anaponyedwa miyala, anacekedwa pakati, anayesedwa, anaphedwa ndi lupanga, anayendayenda obvala zikopa zankhosa, ndi zikopa zambuzi, nakhala osowa, osautsidwa, ocitidwa zoipa,

Werengani mutu wathunthu Ahebri 11

Onani Ahebri 11:37 nkhani