Ahebri 12:9 BL92

9 Komanso, tinali nao atate a thupi lathu akutilanga, ndipo tinawalemekeza; kodi sitidzagonjera Atate wa mizimu koposa nanga, ndi kukhala ndi moyo?

Werengani mutu wathunthu Ahebri 12

Onani Ahebri 12:9 nkhani