Ahebri 13:11 BL92

11 Pakuti matupi a nyama zija, mwazi wa izo umatengedwa ndi mkulu wa ansembe kulowa m'malo opatulidwa, cifukwa ca zoipa, amatenthedwa kunja kwa tsasa.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 13

Onani Ahebri 13:11 nkhani