Amosi 6:14 BL92

14 Pakuti taonani, ndidzakuutsirani mtundu wa anthu, nyumba ya Israyeli, ati Yehova Mulungu wa makamu; ndipo adzakupsinjani kuyambira polowera ku Hamati kufikira mtsinje wa kucidikha.

Werengani mutu wathunthu Amosi 6

Onani Amosi 6:14 nkhani