Ezara 1:11 BL92

11 Zipangizo zonse zagolidi ndi zasiliva ndizo zikwi zisanu ndi mazana anai. Izi zonse Sezibazara anakwera nazo, pokwera andende aja kucokera ku Babulo kumka ku Yerusalemu.

Werengani mutu wathunthu Ezara 1

Onani Ezara 1:11 nkhani