Ezara 9:5 BL92

5 Ndi pa nsembe yamadzulo ndinanyamuka m'kuzunzika kwanga, cobvala canga ndi maraya anga zong'ambika; ndipo ndinagwada ndi maondo anga, ndi kutambasula manja anga kwa Yehova Mulungu wanga;

Werengani mutu wathunthu Ezara 9

Onani Ezara 9:5 nkhani