Hoseya 10:14 BL92

14 Momwemo phokoso lidzaukira anthu ako, ndi malinga ako onse adzapasuka, monga Salimani anapasula Betaribeli; tsiku la nkhondo amai anaphwanyika pamodzi ndi ana ace.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 10

Onani Hoseya 10:14 nkhani