Mlaliki 2:10 BL92

10 Ndipo ciri conse maso anga anacifuna sindinawamana; sindinakaniza mtima wanga cimwemwe ciri conse pakuti mtima wanga unakondwera ndi nchito zanga zonse; gawo langa la m'nchito zanga zonse ndi limeneli.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 2

Onani Mlaliki 2:10 nkhani