Mlaliki 2:19 BL92

19 Ndipo ndani adziwa ngati adzakhala wanzeru pena citsiru? Koma adzalamulira nchito zanga zonse ndinasauka nazo, ndi kuzigwira mwanzeru kunja kuno. Icinso ndi cabe.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 2

Onani Mlaliki 2:19 nkhani