21 Pakuti pali munthu wina agwira nchito mwanzeru ndi modziwa nadzipinduliramo; koma adzapereka gawo lace kwa munthu amene sanagwirapo nchito. Icinso ndi cabe ndi coipa cacikuru.
Werengani mutu wathunthu Mlaliki 2
Onani Mlaliki 2:21 nkhani