Mlaliki 2:3 BL92

3 Ndinafuna mumtima mwanga kusangalatsa thupi langa ndi vinyo, mtima wanga ulikunditsogolera mwanzeru, ndi kugwira utsiru, kuti ndizindikire cabwinoco ca ana a anthu nciani cimene azicicita pansi pa thambo masiku onse a moyo wao.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 2

Onani Mlaliki 2:3 nkhani