Mlaliki 9:3 BL92

3 Ici ndi coipa m'zonse zicitidwa pansi pano, cakuti kanthu kamodzi kagwera onse; indetu, mtimanso wa ana a anthu wadzala udio, ndipo misala iri m'mtima wao akali ndi moyo, ndi pamenepo apita kwa akufa.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 9

Onani Mlaliki 9:3 nkhani