Zekariya 11:6 BL92

6 Pakuti sindidzacitiranso cifundo okhala m'dzikomo, ati Yehova; koma taonani, ndidzapereka anthu, yense m'dzanja la mnansi wace, ndi m'dzanja la mfumu yace; ndipo iwo adzakantha dzikoli, ndi m'dzanja mwao sindidzawalanditsa.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 11

Onani Zekariya 11:6 nkhani