Zekariya 6:13 BL92

13 inde adzamanga Kacisi wa Yehova; nadzasenza ulemererowo, nadzakhala ndi kulamulira pa mpando wacifumu wace; nadzakhala wansembe pampando wacifumu wace; ndi uphungu wa mtendere udzakhala pakati pa iwo awiri,

Werengani mutu wathunthu Zekariya 6

Onani Zekariya 6:13 nkhani