Ahebri 9:10 BL92

10 Popeza akhala zoikika za thupi zokha (ndi zakudya, ndi zakumwa, ndi masambidwe osiyana-siyana), oikidwa kufikira nthawi yakukonzanso.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 9

Onani Ahebri 9:10 nkhani