Hoseya 4:1 BL92

1 Imvani mau a Yehova, inu ana a Israyeli; pakuti Yehova ali ndi mlandu ndi okhala m'dziko, popeza palibe coonadi, kapena cifundo, kapena kudziwa Mulungu m'dziko.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 4

Onani Hoseya 4:1 nkhani