Mlaliki 3:22 BL92

22 M'mwemo ndinazindikira kuti kulibe kanthu kabwino kopambana aka, kuti munthu akondwere ndi nchito zace; pakuti gawo lace ndi limeneli; pakuti ndani adzamfikitsa kuona comwe cidzacitidwa ataca iyeyo?

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 3

Onani Mlaliki 3:22 nkhani