Mlaliki 4:1 BL92

1 Ndinabweranso tsono ndi kupenyera nsautso zonse zimacitidwa kunja kuno; ndipo taona, misozi ya otsenderezedwa, koma analibe wakuwatonthoza; ndipo akuwatsendereza anali ndi mphamvu koma iwowa analibe wakuwatonthoza.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 4

Onani Mlaliki 4:1 nkhani