Mlaliki 5:1 BL92

1 Samalira phazi lako popita ku nyumba ya Mulungu; pakuti kuyandikira kumvera kupambana kupereka nsembe za zitsiru; pakuti sizizindikira kuti zirikucimwa.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 5

Onani Mlaliki 5:1 nkhani