2 Usalankhule mwanthuku mtima wako, usafulumire kunena kanthu pamaso pa Mulungu; pakuti Mulungu ali kumwamba, iwe uli pansi; cifukwa cace mau ako akhale owerengeka.
Werengani mutu wathunthu Mlaliki 5
Onani Mlaliki 5:2 nkhani