Mlaliki 8:17 BL92

17 pamenepo ndinaona nchito zonse za Mulungu kuti anthu sangalondole nchito ziciddwa pansi pano; pakuti angakhale munthu ayesetsa kuzifunafuna koma sadzazipeza; indetu ngakhalenso wanzeru akati, ndidziwa, koma adzalephera kuzilondola.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 8

Onani Mlaliki 8:17 nkhani