Mlaliki 9:1 BL92

1 Pakuti zonsezi ndinazisunga mumtima ndikalondoletu zonsezi; kuti olungama ndi anzeru ndi nchito zao ali m'manja a Mulungu; ngakhale kukonda ngakhale kudana anthu sadziwa; zonse ziri m'tsogolo mwao.

Werengani mutu wathunthu Mlaliki 9

Onani Mlaliki 9:1 nkhani