Zekariya 1:12 BL92

12 Ndipo mthenga wa Yehova anayankha nati, Yehova wa makamu, mudzakhala mpaka liti osacitira cifundo Yerusalemu, ndi midzi ya Yuda, imene munakwiya nayo zaka izi makumi asanu ndi awiri?

Werengani mutu wathunthu Zekariya 1

Onani Zekariya 1:12 nkhani