Zekariya 12:3 BL92

3 Ndipo kudzacitika tsiku ilo, ndidzaika Yerusalemu akhale mwala wolemetsa mitundu yonse ya anthu; onse akuusenza adzadzilasa nao; ndi amitundu onse a pa dziko lapansi adzasonkhana kutsutsana nao.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 12

Onani Zekariya 12:3 nkhani