Zekariya 12:4 BL92

4 Tsiku ilo, ati Yehova, ndidzakantha kavalo ali yense ndi kumdabwitsa, ndi womkwera adzayaluka; ndipo ndidzatsegulira maso anga nyumba ya Yuda, ndi kukantha kavalo ali yense wa mitundu ya anthu akhale wakhungu.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 12

Onani Zekariya 12:4 nkhani