Zekariya 13:6 BL92

6 Ndipo wina akati kwa iye, Zipsera izi m'manja mwako nza ciani? adzayankha, Ndizo za mabala anandilasa m'nyumba ya ondikonda.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 13

Onani Zekariya 13:6 nkhani