Zekariya 13:7 BL92

7 Galamuka, lupanga, pa mbusa wanga, ndi pa munthu mnzanga wa pamtima, ati Yehova wa makamu; kantha mbusa, ndi nkhosa zidzabalalika; koma ndidzabwezera dzanja langa pa zazing'onozo.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 13

Onani Zekariya 13:7 nkhani