8 Pakuti atero Yehova wa makamu: Utatha ulemererowo ananditumiza kwa amitundu amene anakufunkhani; pakuti iye wokhudza inu, akhudza mwana wa m'diso lace.
Werengani mutu wathunthu Zekariya 2
Onani Zekariya 2:8 nkhani