Zekariya 3:7 BL92

7 Atero Yehova wa makamu: Ukadzayenda m'njira zanga, ndi kusunga udikiro wanga, pamenepo udzaweruza nyumba yanga, ndi kusunga mabwalo anga, ndipo ndidzakupatsa malo oyendamo mwa awa oimirirapo.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 3

Onani Zekariya 3:7 nkhani