Zekariya 3:8 BL92

8 Tamvera tsono, Yoswa mkulu wa ansembe, iwe ndi anzako akukhala pansi pamaso pako; pakuti iwo ndiwo cizindikilo; pakuti taonani, ndidzafikitsa mtumiki wanga, ndiye Mphukira.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 3

Onani Zekariya 3:8 nkhani