Zekariya 7:12 BL92

12 Inde, anasanduliza mitima yao ikhale ngati mwala woti gwa, kuti angamve cilamulo, ndi mau amene Yehova wa makamu anatumiza ndi Mzimu wace mwa aneneri oyamba aja; m'menemo munafuma mkwiyo waukuru wocokera kwa Yehova wa makamu.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 7

Onani Zekariya 7:12 nkhani