Zekariya 7:14 BL92

14 koma ndidzawabalalitsa ndi kabvumvulu mwa amitundu onse amene sanawadziwa. Motero dziko linakhala bwinja, m'mbuyo mwao; palibe munthu wopitapo ndi kubwererako; pakuti adaika dziko lofunikalo labwinja.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 7

Onani Zekariya 7:14 nkhani