Zekariya 8:9 BL92

9 Atero Yehova wa makamu: Alimbike manja anu, inu akumva masiku ano mau awa pakamwa pa aneneri amene anakhalako tsiku lakuikidwa maziko a nyumba ya Yehova wa makamu, ndiyo Kacisi, kuti amangidwe.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 8

Onani Zekariya 8:9 nkhani