Zekariya 9:7 BL92

7 Ndipo ndidzacotsa mwazi wace m'kamwa mwace, ndi zonyansa zace pakati pa mano ace; momwemo iyenso adzakhala wotsalira wa Mulungu wathu, ndipo adzakhala ngati mkuru wa pfuko m'Yuda, ndi Ekroni ngati Myebusi.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 9

Onani Zekariya 9:7 nkhani