Zekariya 9:8 BL92

8 Ndipo ndidzamangira nyumba yanga misasa, kuiletsera nkhondo, asapitepo munthu kapena kubweranso; ndipo wakuwasautsa sadzapitanso pakati pao; pakuti tsopano ndapenya ndi maso anga.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 9

Onani Zekariya 9:8 nkhani