Danieli 11:10 BL92

10 Ndi ana ace adzacita nkhondo, nadzamemeza makamu a nkhondo akuru ocuruka, amene adzalowa, nadzasefukira, nadzapita; ndipo adzabwerera, nadzacita nkhondo mpaka linga lace.

Werengani mutu wathunthu Danieli 11

Onani Danieli 11:10 nkhani