Danieli 11:20 BL92

20 Ndipo m'malo mwace adzauka wina wakupititsa wamsonkho pa ulemerero wa ufumuwo; koma atatha masiku owerengeka adzatyoledwa iye, si mwamkwiyo, kapena kunkhondo ai.

Werengani mutu wathunthu Danieli 11

Onani Danieli 11:20 nkhani