Danieli 3:12 BL92

12 Alipo Ayuda amene munawaika ayang'anire nchito ya dera la ku Babulo, Sadrake, Mesake, ndi Abedinego, amuna awa, mfumu, sanasamalira inu, satumikira milungu yanu, kapena kulambira fano lagolidi mudaliimikalo.

Werengani mutu wathunthu Danieli 3

Onani Danieli 3:12 nkhani