Danieli 4:35 BL92

35 ndi okhala pa dziko lapansi onse ayesedwa acabe; ndipo Iye acita mwa cifunito cace m'khamu la kumwamba ndi mwa okhala pa dziko lapansi; ndipo palibe woletsa dzanja lace, kapena wakunena naye, Mucitanji?

Werengani mutu wathunthu Danieli 4

Onani Danieli 4:35 nkhani