Danieli 7:20 BL92

20 ndi za nyanga khumi zinali pamutu pace, ndi nyanga yina Idaphukayi, imene zidagwa zitatu patsogolo pace; nyangayo idali ndi maso ndi pakamwa pakunena zazikuru, imene maonekedwe ace anaposa zinzace.

Werengani mutu wathunthu Danieli 7

Onani Danieli 7:20 nkhani