Danieli 8:2 BL92

2 Ndipo ndinaona m'masomphenya; tsono kunali, pakuwaona ine ndinali m'Susani, m'nyumba ya mfumu, ndiwo m'dziko la Elamu; ndinaona m'masomphenya kuti ndinali kumtsinje Ulai.

Werengani mutu wathunthu Danieli 8

Onani Danieli 8:2 nkhani