24 Ndi mphamvu yace idzakhala yaikuru, koma si mphamvu yace yace ai, nidzaononga modabwiza, nidzakuzika, ndi kucita, ndi kuononga amphamvuwo, ndi anthu opatulikawo.
Werengani mutu wathunthu Danieli 8
Onani Danieli 8:24 nkhani