1 Pemphani kwa Yehova mvula, m'nyengo ya mvula ya masika, kwa Yehova wolenga mphezi; ndipo adzawapatsa mibvumbi ya mvula, kwayense zophukira kuthengo.
Werengani mutu wathunthu Zekariya 10
Onani Zekariya 10:1 nkhani