2 Pakuti aterafi anena zopanda pace, ndi aula aona bodza; nafotokoza maloto acabe, asangalatsa nazo zopanda pace; cifukwa cace ayendayenda ngati nkhosa, azunzika popeza palibe mbusa.
Werengani mutu wathunthu Zekariya 10
Onani Zekariya 10:2 nkhani