Zekariya 8:23 BL92

23 Atero Yehova wa makamu: Kudzacitika masiku awo amuna khumi adzagwira, ndiwo a manenedwe onse a amitundu, inde adzagwira mkawo wa munthu ali Myuda, ndi kuti, Tidzamuka nanu, pakuti tamva kuti Mulungu ali ndi inu.

Werengani mutu wathunthu Zekariya 8

Onani Zekariya 8:23 nkhani